Sat. Apr 20th, 2024

Boma Likufuna Kuthetsa Nkhanza Zomwe A Traffic Akumachita Mudziko Lino

By Suleman Chitera Sep13,2022

Boma sopano lazindikila zoti a traffic ambili akugwila ntchito ndi akuluakulu achipani cha DPP kuti awononge mbiri ndikuligwesa.

Pofuna kuwonesa kuti eni magalimoto maka eni ma minibus sakuchitidwa nkhaza boma sopano layamba kufufuza apolice a traffic omwe akumagwila magalimoto mwachisawawa maka omwe akumakhala nditimilandu tating’ono kwambili monga kuyiwala ma triangle plates.

Kafukufukuyi akuza antolankhani a Malawians News Online atabwelesa poyela malipoti onena kuti a traffic ambili maka omwe akumayima mumadela ozungulira mzinda wa Blantyre, Lilongwe ndi Chiradzulu akumachitila nkhanza oyendesa ma minbus komanso magalimoto ang’onoang’ono pomawalipilitsa ndalama zambili zedi pamilandu yaying’ono kwambili yomwe akanangotha kuwapasa chenjezo.

Milandu Yoyenera kulipira pa Nsewu ndi Iyi

Milandu yoyenela kugwidwa pansewu imayenela kukhala ikuluikulu monga kuyendesa galimoto opanda Insurance, Licence, COF, Overload ndikuyendesa galimoto utalezela kapena galimoto yamatayala.

Milandu ing’onoing’ono a traffic amangoyelenela kupeleka chenjezo basi osati mpaka kugwila ndikudulira ma driver lisiti ya K10 000 kuti akalipile.

Nkhanza zomwe a traffic amenewa akuchita ndizosayenela mudziko lino kamba koti zikusoneza kwambili ubale wa anthu, eni magalimoto ndi boma.

Related Posts
Mumba Should Clear Himself On The Alledged Corrupt Dealings Alongside Chinese Companies

Alot has been said regarding corrupt undertakings by one Engineer Vitumbiko Mumba who is on a mission to enrich himself Read more

ACB Boss Martha Chizuma Too Stubborn  

A group of Mbadwa zokhudzidwa za Malawi has raised concern with what they have described as “continued stubbornness” of Anti-Corruption Read more

Biased Mainstream Malawi Media jealously overrating Martha Chizuma while criminating Zuneth Sattar

By Deus Chikalaza The truth be told that mainstream (conversional) Malawi media including Malawi Broadcasting Cooperation (MBC) Nation Newspaper, Times Read more

Martha Chizuma’s ACB Substandard Report Backfires, Chakwera Deceived

Chilima, Kapondamgaga be reinstated Zuneth Sattar To Be Apologised When President Lazarus Chakwera described Anti-Corruption Bureau (ACB) Director General Martha Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation