Thursday, March 28
Shadow

Chakwera Atsitse Mtengo Wa Fertiliser Kuchoka Pa k15,000 Kufika Pa k7500

Bungwe la CDEDI Malawi lalamula kuti mtsogoleri wadziko lino Lazarus Chakwera atsitse mtengo wafeteleza yemwe ali pansi pa zipangizo za ulimi zotsika mtengo.

Mkulu wa bungwe la CDEDI Sylvester Namiwa amalankhula ndi atolankhani lachinayi mumzinda wa Lilongwe.

Malingana ndi Namiwa, a Chakwera akuyenera kutsitsa mtengo wafetelezayu kuchoka pa MK15 000 kufika pa MK7500 pathumba asanakhazikitse ndondomeko yogulira zipangizo za ulimi zotsika mtengo pa 21 November.

Mtsogoleri wabungwe la CDEDI-yu wachenjezanso boma kuti lisagulitse feteleza amene dziko la Malawi lalandira ngati thandizo kuchokera ku maiko ena, ndipo mmalo mwake agawe wa ulele kwa a Malawi.

A Namiwa alamulanso boma kuti litsekule misika yonse ya Admarc ndicholinga chakuti a Malawi asavutike kugula zipangizo za ulimi zotsika mtengo chaka chino.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation