Sun. Apr 28th, 2024

Chilima akhoza kudikira madzi amphutsi”- atero Dr. Chaima

Katswiri pa nkhani za ndale ndi ulamuliro wabwino mdziko muno a Dr George Chaima alangiza wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino a Dr Saulos Chilima kuti ayambe kukonzekela zodzayima pa chisankho cha chaka cha mawa ngati mtsogoleri wa chipani cha UTM posatengera za mgwirizano omwe ulipo pakatipa iwo ndi Dr. Lazarus Chakwera.

A Chaima ati a Chilima achedwa akadalira kwambiri mgwirizano wawo omwe anagwirizana pa zisankho za chaka cha 2020.

Malingana ndi a Chaima ati zomwe chapanga chipani cha Malawi Congress, kunena kuti Dr. Chakwera adzayimira ngati mtsogoleri wachipanichi chaka cha mawa sikulakwa kuli konse.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

The British NCA Operations In Malawi Remain Questionable, Britons Aim To Topple Tonse Government

Exposed! British NCA bankrolls PIJ to victimize successful business persons, politicians, judges in Malawi The truth be told! The establishment Read more

Mirece supports land reclamation bought by foreigners

Reverend Flywell Somanje…. this is the way to go A governance and human rights organization, the Millennium Information and Resource Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open