Mon. Apr 29th, 2024

Oletsetsa ndewu savula shati–Chilima

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa dziko lino a Saulos Chilima wafika mu nzinda wa Mzuzu madzulo ano pomwe mawa Lamulungu akuyenera kukhala nawo pa mwambo okumbukira a malitili omwe uchitikire m’boma la Nkhata Bay.

Anthu ochuluka anasonkhana pa Roundabout ya Shoprite kudikira a Chilima kuti awayankhule.

Koma iwo anayamika anthuwa powadikira ndipo anamaliza ndi mwambi omwe oti: ‘Oletsetsa ndewu savula shati’

Ena mwa omwe anawalandira a Chilima ndi nduna ya zokopa alendo a Vera Kamtukule ndi atsogoleri ena a chipani cha UTM mchigawo chakumpoto komanso mfumu ya nzinda wa Mzuzu a Gift Desire Nyirenda.

Dr Chilima

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

AGHF Feeds Patients, Guardians At Mangochi District Hospital

A giving hand foundation is a local organisation working in various programs in Malawi. On Thursday the organization together with Read more

NBM Donates K100 Million Towards Forest Restoration

National Bank of Malawi has committed K100 million for preservation and restoration of 6 natural resources in the country by Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open