Saturday, September 30Malawi's top news source
Shadow

Diso La Ndale Likuona Patali Pomwe A Muluzi Akhululukidwa Milandu

50 + 1 Ndi nambala yomwe aliyense ali nayo mmaganizo mwake Maka Maka anzathu andalewa. Poganizila kuti nyengo yofuna kukopa a mphevu dyera kunthikofe yayandikira.

Inde poti ndale nkugwetsana zipani zakangalika kulimbitsa zipaninzawo mmadera osiyanasiya, posachedwapa tawona chipani cha afford chikukangalika kuchititsa misonkhano yake Madera osiyanasiyana, ponena akumati ndi misonkhano yachikondwerero kuti akwanitsa zaka zochuluka chikhazikitsireni chipani chawo. tinaona nkhwimbi la anthu linali kumeneko komanso tinamva mfundo zawo iwotu ulendo uno sakulabada za munthu koma mtsogoleri wawo a Enock chihana ayima paokha popeza iwo atopa kutsogoza atsogoleri ena omwe akalowa muboma sakuchita zomwe amalawi akufuna.
Diso la ndale layang’ana pa 50 +1 kuti kodi afford ngati imakanika popandala lamulori kuwina kodi pano pomwe 50+1 ali m’bwalo afford ingadutse? Tinene mosabitsa afford siyani kulota panganibe mgwilizano ndi chipani cha kumtima kwanu kuti mukhale m’boma kapena kuti muzapezeko unduna. Kupanda kutero Diso landale silikukuonani 2025.

KU DPP

Kumbali ya DPP chidwi cha Diso la ndale chagona pa chisankho chawo chomwe achititse chosankha mtsogoleli wachipani chawo. Kumeneku kuli anthu angapo omwe akupikisana, adadi tiwayiwale ndi munthu odekha iwo sangapangenso dala chibwana chofuna kuimira, pakadali pano akhala dala chete kufuna kuti asagawanitse chipani akanena kuti saimira kapena akasankhiratu munthu. Koma angakhale tikudziwa zofuna zawo koma kupanga chibwana chosiya Kondwani Nankhumwa pa udindo wawo juzakhala kutha kwa chipani ngati makatani. Ndalama ndi kutchuka ndizosiyana pandale, kabambe atha kukhala wa chuma koma mfundo za ndale alibe kumusankha iye ilo ndi bomba mwazitchera nokha, kumeneko kodwani nankhumwa ndiye jokala wanu. Iye atha kukhala opanda ndalama kuyerekeza ndi enawa koma ali ndi mfundo pa ndale, zili ndi inu kutola Jokala yu kapena ayi

MCP VS UTM

Mgwedegwede uli pakati pa zipani ziwilizi. Kodi atsogolele amalawi ndi ndani? Tinene mosabisa pano bomali ndi la mgwilizano Kaya mukwiya kapena ayi chifukwa munasokherana a zipani ziwirinu. Aliyense payekha anakanika mu 2019, munatenga bomali kamba ka malamulo chifukwa khoti linagamula kuti chisankho chinayendetsedwa mosasata malamulo. Chipani cha MCP mosabisa chakhala chikunena kuti iwo mtsogoleri wawo ndi Chakwela ndipo mosabisa UTM mtsogoleri wawo ndi Chilima, Koma chomwe sitikudziwa ndi chakuti mgwilizano wa Tonse ukhalapo? Ngati utakhalepo atsogolere ndani?

Mukuona kwa Diso la ndale chipani cha MCP chikuponyera mbedza kwa Kuya, zomwe zachitika lero pokhululukira a Bakili muluzi pa mlandu wawo ndi chizindikilo chimodzi kuti MCP ikufuna kuzakhala pa mgwilizano ndi UDF. Ndi akufuna kuzagwilitsa ntchito mwana wa amuluzi ngati wachiwiri wawo. Munthu wamba ngati inu ndi ine sungazimvetse koma ukakhala ndi diso la ndale uzimvetsa, Duso la ndale linayambabkuona izi kale kale tonse Italian muboma pomwe qmuluzi amatumizidwa kunja kuhaimira a chakwera, kenakom mkumano wawo pa namondwe wa Freddy. lero ndi lero boma kuzangozambatuka nkuneba kuti taunikira mulanduwu tawona kuti ulibe tsogolo. Zoona pa zaka 14 lero limenero kuona kuti mulandu wakuba 1.7 billion ulibe tsogolo.

Ndale nkutcherana ndiye Chipani cha UTM chikuyenera kusamala chifukwa chizazindiikira chili mu dzenje ngati sichikhala ndi Diso la ndale . A UTM sakudera nkhawa chifukwa chipani chonse chomwe chagwilizana ndi UDF sichinawinepo masankho. Ndipo MCP iziwe kuti pa ndale palibe mdani weniweni UTM NDI DPP atha kuzagwlizananso. Cholinga chofuna kugwersa MCP .

Kukhala chete kwa chilima kukudetsa nkhawa ambiri otsatila chipanichi ndipo akufunitsitsa atamva maganizo ake koma poti ndale nkutcherana UTM ndi utsogoleri wawo nawo palipo pomwe aponda mwala.

Andale samalani ndipo khalani ndi DISO LA NDALE

DR MWALE

Related News
Lets Not Forget Why US/British Killed Muammar Gaddafi?

Gaddafi was certainly not killed for humanitarian reasons. He wanted to empower Africa. He had a plan to create a Read more

DoDMA’S IPDC MUST BE INVESTIGATED OVER THE UNPROCEDURAL AND BIASED AWARDMENT OF CONTRACT.

Story by a concerned bidder Yamikani Nicholas Kachingwe. The Department of Disaster Management(DoDMA) an institution under the office of the Read more

Religious Faith Are Masters Of Pastoral Letters And Corruption

Malawian churches are the masters of pastoral letters. Both CCAP and Catholics are well known for producing the best pastoral Read more

ACB And Ombudsman Is Totally Different Analyst Tells Martha Chizuma

By Chikuluwaza Political Contributor Resign is better than being fired In fact ACB is totally different from Ombudsman where Martha Read more

LAWYER ACCUSE CHAKWERA AND MCP GOVERNMENT OF KICKING FREEDOM OF EXPRESSION.

Counsel Khumbo Soko Writes: That the Constitutional right to freedom of expression covers even the right to publish offensive material Read more

Sattar Is Just A Sheer Scapegoat, Curing Symptom To Temporarily Hide The Pain

By Apawo Kwayera WHY BASHING SATTAR IS JUST CURING SYMPOTOMS Social media activists—mostly Idriss Ali Nassah, Onjezani Kenani, Joshua Mbere Read more

Martha Chizuma Isn’t Above The Law, Let Legality And Constitutionalism Prevail

Opinion by James Kayuni, student of law at University of Nairobi in Kenya. There is, of course, something questionable about Read more

Under Chizuma’s Leadership, Is There Anything Tangible ACB Can Show?

By Attwell Chilangambwa Soon, Martha Chizuma's contract as the boss at the Anti-Corruption Bureau (ACB) will be expiring and debate Read more

Is jealousy, personal vendetta driving Malawi social media influencers hatred against businessman Sattar?

If you read what people such as Onjezani Kenani, Kondwani Munthali, Idris Ali Nassah and Joshua Mbele posts on social Read more

NCA Report Against Sattar Is A Hearsay No Proof Of Evidence, Sattar’s Lawyers Ready To Challenge In Court

By Jivason Kazipatike I have seen extracts of a document purported to have been filed by National Crimes Agency in Read more

News To Read

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *