Mgwilizano Wa Tonse Walephera Kukwanilisa Malonjezo

Akatswiri adzudzula boma la mgwirizano wa Tonse ati kamba kosakwaniritsa ena mwa malonjeza omwe unapereka kwa a Malawi usanalowe m’boma.

Izi zikubwera pomwe patha zaka zitatu dziko lino litachititsa chisankho chamtsogoleri chachibweleza pa 23 June mchaka cha 2020.

Moses Mkandawire, Wapampando wa bungwe la National Anti-Corruption Alliance, wati pakhala pali nkhani zakatangale zokhudza akuluakulu ena aboma.

Mkandawire wati izi ndi chifukwa choti bomali silikuikila chidwi chenicheni chithana ndi mchitidwe wa katangale.

Mkuikilapo ndemanga yake George Phiri katswiri pa nkhani za ndale wati kulephela kwa boma la mgwilizano wa Tonse kukwanilitsa zomwe linalonjeza kukukwiitsa amalawi

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window