Tuesday, March 19
Shadow

ONYAMULA MAKALA AMUNJATA KU SALIMA

Apolisi ku Salima amanga bambo wa zaka 30, Yotamu Mapulanga pomuganizira kuti amazembetsa makala ndipo amulandanso galimoto yomwe ananyamulira makalawo ponena kuti inalibe kalata zoyenera.

M’neneri wa apolisi m’bomalo, Sub-Inspector Jacob Khembo wati apolisi alanda galimoto ya 15 ton ya mtundu wa Scania yomwe nambala yake ndi KK 7020, yomwe inali yodzadza ndi matumba a makala.

Sub-Inspector Khembo wati apolisi anagwira mkukuyu anthu ena atawatsina khutu koma pano ntchito yofufuza ili mkati kuti agwire anthu ena omwe athawa.

Mapulanga amachokera m’mudzi wa Chilipa, mfumu yaikulu Chimwala, m’boma la Mangochi.

Iye akawonekera ku bwalo zofufuza za apolisi zikatha.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation