Fri. Apr 19th, 2024

Sindingalowe UTM yomwe ili ndi aphungu anayi – Nankhumwa

Wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipani cha Democratic Progressive Party (DPP) kumwera Kondwani Nankhumwa wanena mphekesera zoti akufuna kugulitsa chipanichi ku UTM kapena Malawi Congress Party (MCP).

A Nankhumwa amalankhula izi dzulo ku Lilongwe pa Mgona ground pomwe adachita msonkhano wa ndale.

Adayankha mphekesera zomwe zidamveka zoti akadzapambana kukhala Purezidenti wa DPP Nankhumwa alowa UTM kapena MCP.

Malinga ndi a Nankhumwa sangalowe UTM yomwe ili ndi aphungu anayi okha ku Nyumba ya Malamulo.

Adapitiliza kunena kuti iye ndi DPP ndipo sakuganiza zolowa chipani china chilichonse.

Malinga ndi a Nankhumwa ati adzapikisana nawo pa mpando wa utsogoleri kumsonkhanowu ndipo apambana ndi 95%.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation