Nkhani Za Fertilizer Ku Dowa Central East
By Rev. Flywell Somanje. Malinga ndikafuku yemwe wachitika ndi Bungwe la MiRECE, mosemunja yambikira tchito yongawa fertilizer Dziko Muno athu odzungulira Dowa Boma sanapezebe fertilizer mpaka lero, chikuyimitsa mutu athu ndi chakuti apa ndi pa mchombo pa Boma la Dowa, Koma fertilizer akungawidwa kwambiri kumandera komwe ma MP akuchokera, ku Mvera komwe akuchokera MP chimwendo, […]