Gulu lina latimu yampira wamiyendo yadziko lino ya The Flames lanyamuka ulendo waku Burkina Faso kukatenga mbali mundime yodzigulira malo mumpikisano wa AFCON.
Gululi lanyamuka pabwalo landege ku Lilongwe.
Anyamatawa akukakumana ndi gulu lachiwiri la anzawo ku Ethiopia ndikupitiliza ulendo wawo kudzera m’dziko la Mali.
Timuyi, yomwe yagonja dzulo ndi Burundi, ikumana ndi Burkina Faso lachiwiri lino.
Sponsored • Malawi Freedom Network
MALAWI
FREEDOM
NETWORK
United for Freedom, Justice and a Better Malawi
Airtel Money
0994095804
Mpamba
0881428759
BANK TRANSFER
FDH Bank
Acc No:
1400000670385NBS Bank
Acc No:
10118988Thank you for your support!
