FB IMG 1725608391884FB IMG 1725608391884

Gulu lina latimu yampira wamiyendo yadziko lino ya The Flames lanyamuka ulendo waku Burkina Faso kukatenga mbali mundime yodzigulira malo mumpikisano wa AFCON.

Gululi lanyamuka pabwalo landege ku Lilongwe.

Anyamatawa akukakumana ndi gulu lachiwiri la anzawo ku Ethiopia ndikupitiliza ulendo wawo kudzera m’dziko la Mali.

Timuyi, yomwe yagonja dzulo ndi Burundi, ikumana ndi Burkina Faso lachiwiri lino.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  Peter Mponda returns to FCB Nyasa Big Bullets as Head Coach

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *