Flames yawuyatsa waku Burkina Faso
Gulu lina latimu yampira wamiyendo yadziko lino ya The Flames lanyamuka ulendo waku Burkina Faso kukatenga mbali mundime yodzigulira malo mumpikisano wa AFCON.
Gululi lanyamuka pabwalo landege ku Lilongwe.
Read also: DPP Expresses Surprise Over Chakwera’s New Fertilizer Price Announcement
Read also: Austerity Measures in Question as president Chakwera embarks on another foreign trip
Read also: MCP Supporter Admits Party’s Waning Ground Support Amid Mounting Frustrations
Anyamatawa akukakumana ndi gulu lachiwiri la anzawo ku Ethiopia ndikupitiliza ulendo wawo kudzera m’dziko la Mali.
Timuyi, yomwe yagonja dzulo ndi Burundi, ikumana ndi Burkina Faso lachiwiri lino.
Read also: Demolitions begin as Malawi prepares to rebuild dilapidated Liwonde-Matawale road
Read also: Hajj 2026 Peaks as 1.5 Million Muslims Gather at Arafat
Read also: Calls Grow for Accountability as Chakwera Promises to Expose NOCMA Saboteurs





