Tiyikizeni mu ma Pemphero A Malawi – wapempha ma Mabedi
Mphunzitsi wamkulu watimu ya Flames Patrick Mabedi wapempha nzika zadziko lino kuti ziwayikize mu mapemphero ati pofuna kupeza chipambano mumasewero awo mawa ndi Burkina Faso mumasewero ofuna kudzigulira malo ku ndime yotsiliza ya Africa Cup of Nations ( AFCON) omwe achitikire ku Mali. Mabedi wati timu yake ikamapita mumasewerowa ifunitsitsa kupeza chipambano ati pofuna kuziziritsa […]