FB IMG 1726055642282

Timu ya Premier Bet Dedza Dynamos yalengeza zakubwereranso kuchisa kwa katswiri wa kutsogola, Promise Kamwendo, yemwe anautsa mpungwe-mpungwe pa msika ogula ndi kugulitsa osewera m’dziko muno.

Izi zikudza kutsatira chigamulo cha bungwe la Football Association of Malawi (FAM) chomwe linapereka kuti katswiriyu akuyenera kubwerera ku timuyi kamba kosatsata ndondomeko.

Kamwendo wapanga nawo zokonzekera ku timuyi pamene ikuyembekezeka kusewera ndi timu ya Creck Sporting pa bwalo la Dedza mu ligi ya TNM kumapeto a sabatayi.

Katswiriyu ali ndi zigoli zisanu ndi chimodzi mu ligi ya TNM pamasewero 13 omwe anasewera.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  Mabedi names 30-man squad, Gaba dropped again

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *