Tisiye kuloza chala a Mabedi-Mpima
Bungwe la aphunzitsi a mpira wamiyendo m’dziko muno lati silikugwilizana ndi anthu omwe akuloza chala mphunzitsi wa timuyi, Patrick Mabedi, kuti walephera ntchito yake.Tinene chalungamo mwayi wathu ndiwochepa tsopano opita ku AFCON – watero Mabedi
Izi zikutsatira kulephera kuchita bwino kwa Flames pomwe inagonja pa khomo ndi timu ya Burundi 1-0 pa bwalo la Bingu mu nzinda wa Lilongwe, komanso 3-2 ndi timu ya Burkina Faso ku Bamako m’dziko la Mali mumpikisano wa Africa Cup of Nations (AFCON).Mend Fences With Gaba -Kinnah Phiri advise Mabedi
Read also: MTUMODZI OPENS 27TH RAC MEETING FOR SADC MEDIA AWARDS
Read also: NBM plc fires up Scorchers ahead of AFCON qualifiers
Read also: MMGA’s Bonface Joseph Leads Charge to Address Chikwawa Water Crisis
Mlembi wa bungweli, Dave Mpima, wati kulankhula zonyoza Mabedi sizithandiza kanthu koma kuti mbali zokhudzidwa zikhale pansi ndikupeza njira yoti timuyi iyambirenso kuchita bwino ngati momwe zinaliri m’zaka za 1987 komanso 1988.
Malawi ili pansi mu gulu potengera kuti ilibe chipambano china chilichonse.
Read also: Chakwera’s Tonse to change leadership hands in next 6 months
Read also: The controversial passport contract: A threat to Malawi’s national security
Read also: Kondwani Nankhumwa Officially Presents Nomination Papers for 2025 Presidential Race at BICC





