FB IMG 1726542759484

Bungwe la aphunzitsi a mpira wamiyendo m’dziko muno lati silikugwilizana ndi anthu omwe akuloza chala mphunzitsi wa timuyi, Patrick Mabedi, kuti walephera ntchito yake.Tinene chalungamo mwayi wathu ndiwochepa tsopano opita ku AFCON – watero Mabedi

Izi zikutsatira kulephera kuchita bwino kwa Flames pomwe inagonja pa khomo ndi timu ya Burundi 1-0 pa bwalo la Bingu mu nzinda wa Lilongwe, komanso 3-2 ndi timu ya Burkina Faso ku Bamako m’dziko la Mali mumpikisano wa Africa Cup of Nations (AFCON).Mend Fences With Gaba -Kinnah Phiri advise Mabedi

Mlembi wa bungweli, Dave Mpima, wati kulankhula zonyoza Mabedi sizithandiza kanthu koma kuti mbali zokhudzidwa zikhale pansi ndikupeza njira yoti timuyi iyambirenso kuchita bwino ngati momwe zinaliri m’zaka za 1987 komanso 1988.

Malawi ili pansi mu gulu potengera kuti ilibe chipambano china chilichonse.

Sponsored • Malawi Freedom Network

MALAWI
FREEDOM
NETWORK

United for Freedom, Justice and a Better Malawi

Airtel Money

0994095804

Mpamba

0881428759

BANK TRANSFER

FDH Bank

Acc No:

1400000670385

NBS Bank

Acc No:

10118988

Thank you for your support!

See also  FC Barcelona News; 8 October 2024;

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *