Bungwe la aphunzitsi a mpira wamiyendo m’dziko muno lati silikugwilizana ndi anthu omwe akuloza chala mphunzitsi wa timuyi, Patrick Mabedi, kuti walephera ntchito yake.Tinene chalungamo mwayi wathu ndiwochepa tsopano opita ku AFCON – watero Mabedi
Izi zikutsatira kulephera kuchita bwino kwa Flames pomwe inagonja pa khomo ndi timu ya Burundi 1-0 pa bwalo la Bingu mu nzinda wa Lilongwe, komanso 3-2 ndi timu ya Burkina Faso ku Bamako m’dziko la Mali mumpikisano wa Africa Cup of Nations (AFCON).Mend Fences With Gaba -Kinnah Phiri advise Mabedi
Mlembi wa bungweli, Dave Mpima, wati kulankhula zonyoza Mabedi sizithandiza kanthu koma kuti mbali zokhudzidwa zikhale pansi ndikupeza njira yoti timuyi iyambirenso kuchita bwino ngati momwe zinaliri m’zaka za 1987 komanso 1988.
Malawi ili pansi mu gulu potengera kuti ilibe chipambano china chilichonse.
MALAWI
FREEDOM
NETWORK
United for Freedom, Justice and a Better Malawi
Airtel Money
0994095804
Mpamba
0881428759
FDH Bank
Acc No:
1400000670385NBS Bank
Acc No:
10118988Thank you for your support!