Tidkira Tsiku Lomwe Ayambe Kupanga Zipatso Zoyendera-CDEDI

Bungwe la Centre for Democracy and Economic Development initiatives-CDEDI lati lidikirabe tsiku lomwe nthambi yoona za anthu olowa ndi kutuluka iyambe ntchito yake yopanga ziphaso(Passport).

Komabe mkulu wa bungweli,Sylvester Namiwa wati wokondwera ndi ganizo la nthambi yoona zolowa ndi kutuluka potsitsa mtengo wa e-passport.

Namiwa wati ngakhale ali wokondwa ndi kutsika mtengo wa chiphaso , iye wati ganizo lotsitsa mtengo wa chiphasochi limayenera kuchitika pa nthawi yomwe boma linathetsa mgwirizano wake ndi kampani ya Techno Brain.

Nthambi yoona zolowa ndi kutuluka yalengeza kuti ntchito yopanga ziphaso iyambiraso sabata ino.

Related Posts

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

David Bisnowaty former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country

Political cum and former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country https://youtu.be/S20UYlVcHs8

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window