Thursday, September 21Malawi's top news source
Shadow

BWATO SATSITSILANA PAKATI PA NYANJA”-Micheal Usi

Nduna yowona zokopa alendo yomwenso ndi wachiwiri kwa mtsogoleri wa chipani cha UTM, Michael Usi awuza President Lazarus chakwera kuti chipani cha UTM chilibe lingaliro lotuluka mu mgwilizano wa Tonse alliance ngakhale pali kagulu kena komwe kakufuna zinthu zitero.

A Usi ati kukakamiza chipani cha UTM kutuluka mu mgwilizano wa Tonse mchimodzimodzi kukakamiza munthu kuti atsike mu bwato lili pakati pa nyanja.

A Usi alumbila ponena kuti UTM ipitiliza kulemekeza mgwilizano wa Tonse.

Iwo ayankhula izi pa mwambo okumbukira mtsogoleri oyamba wa dziko lino Dr Hastings Kamuzu Banda Ku Lilongwe.

Poyankhulapo, ndunayi inauzanso Dr chakwera kuti achotse ntchito kagulu kena ka anthu komwe kakufuna kusokoneza boma lake.

Related News
NEEF Customers Demands Their Deposit Back

A group of business people who applied for National Economic Empowerment Fund (Neef) loans in Mzuzu tstormed office premises for Read more

Malawi president under fire for family appointments to cabinet

New 31-member cabinet includes six figures who are related to each other, although not to the president. Malawians have voiced Read more

Police move to protect persons with albinism

Malawi Police Service has engaged traditional healers in Mwanza on how to protect persons with albinism in the district. Speaking Read more

MARTHA CHIZUMA DECLARES WAR AGAINST CHAKWERA: SAYS PRESIDENT, JUDICIARY, ARMY AND POLICE CORRUPT

In a shocking tale to absorb, ACB boss Martha Chizuma has taken her corruption fight against her bosses, openly going Read more

Police in Chitipa district have arrested Kayange who poured hot water on her husband

According to Chitipa Police PRO Gladwell Simwaka, on March 7, 2022 the victim Blair Kuyokwa, 35, returned home in the Read more

Lilongwe Police recover stolen items

Police in Lilongwe have for the second time this month recovered household items and other property worth over 23 million Read more

Police at Bangwe in Blantyre have arrested three suspects

*Police at Bangwe in Blantyre have arrested three suspects and recovered some items they allegedly stole at Namiyango Assemblies of Read more

CSO SPEAKS AGAINST Anti-Ashok Nair Demos: Says they are ‘Criminal’ in Nature

The Citizen Advancement for Economic Revolution has described the anti-Ashok Nair demonstrations scheduled for tomorrow Wednesday as criminal in nature. Read more

M’tengo wa pakete imodzi ya shuga, tsopano ukumafanana ndi wa bread m’modzi

Izi zadza chifukwa bread wakwela mtengo kufika pa 1 000 Kwacha m'modzi , m'magolosale ena. Akuluakulu ena omwe ali ndi Read more

Police Summon Gaffar Over Death Threats

Details have emerged indicating that Malawi Police has summoned Rafik Gaffar of R Gaffar Transport for series of death threats Read more

News To Read

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *