Mon. Apr 29th, 2024

Chipani Cha DPP Chati Chodabwa Kuti Police Sinamange Wina Aliyense Pa Zipolowe Za Ku Lilongwe

Chipani cha Democratic Progressive Party _ DPP chati chikudabwa kuti mpaka pano a polisi sanamangepo munthu wina aliyese yemwe akukhudzidwa ndi zachipongwe zomwe otsatila chipani cha MCP anapangira otsatila Chipani cha DPP ku Lilongwe pa mbowe filling station.

Nkulu osutsa boma kunyumba ya Malamulo a Mary Navicha, ati akudabwa nazo kuti apolisi akugwiritsidwa ntchito ngati achipani m’malo mogwira ntchito yawo yopeleka chitetezo. Chipongwe Chochitika Lachisanu koma mpaka pano palibe yemwe wanjatidwa. ” Ngati a Chakwera akuzitengela Masewera izi zitha kuzayambitsa Nkhondo m’dziko muno” Anatero a Navicha.

A Navicha anapitilira kunena kuti ” Ngati chipani cha DPP tiliso ndi kuthekera koti tikhoza kukwanitsa zomwe akupanga a MCP ku m’chigawo chapakati chawo chomwe koma ife timakonda Mtendere chifukwa Nkhondo simanga mudzi”.

Iwo amalakhula izi pamene amawona ena mwa ovulazidwa pachiwembucho.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

The British NCA Operations In Malawi Remain Questionable, Britons Aim To Topple Tonse Government

Exposed! British NCA bankrolls PIJ to victimize successful business persons, politicians, judges in Malawi The truth be told! The establishment Read more

Mirece supports land reclamation bought by foreigners

Reverend Flywell Somanje…. this is the way to go A governance and human rights organization, the Millennium Information and Resource Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open