Saturday, September 30Malawi's top news source
Shadow

Kodi Cholakwika Ndi Chani Ndi Ulendo Wa A Chakwera Okayankhula Ku America ?

Kunena moona khalidwe lotutana mudzi onse kunka nawo ku America sikuti tiwanamize a Malawi wayamba ndi boma la a Chakwera ai; koma ili ndi khalidwe lonyasa lomwe lakhala likusakaza ndalama za dziko lino ndima President onse omwe akhala akulamulira dziko lino oChakwera asanayambe kulamula dziko lino.

Funso n’kumati kodi chavuta ndichani ndi ulendo wa oChakwera?
Vuto la ulendo wa oChakwera likudza kamba koti pakali pano m’dziko muno mulibe ndalama zakunja zomwe zimathandiza kuti tizitha kugula katundu wakunja ofunikira yemwe sitimatha kupanga m’dziko mwathu muno monga: mafuta agalimoto, mankhwala akuchipatala, chakudya, zovala ndizinthu zina zonse zomwe sizipangidwa ku Malawi kuno.

Funso lina nali: kodi panalibe njira ina kupatula yoti oChakwera ndi owatsatira awo akwere ndege apite akayankhule?

Njira inalipo ndipo yakhala ikugwilitsidwa ntchito chilowereni m’boma oChakwera. Iwo akhala akugwiritsa ntchito Skype ndi njira zina poyankhula pa makina a internet omwe amatenga zomwe akuyankhula ali kuno kumudzi kupita ku America.

Kodi zikanathandiza chani pachuma chathu?
Izi zikanasimikizira mayiko onse kuti dziko lathu likusaukira ndalama yakunja ndipo tikufunika chithandizo chamayiko ena.

Ena onse omwe akukumana nawo amene akuti ndi ma investor zinalinso zotheka kuyankhula nawo panjira iyi.

Izi zikanathandiza kuti ma million a ndalama za America omwe awonongedwa pa ulendowu agwire ntchito zothandiza kupeza katundu yemwe tikuvutika poyitanitsa kunja kamba kakusowa kandalama yakunja pakali pano.

Pomaliza, tiwapemphe a president monga m’busa kuti akumbuke mawu a mfumu Solomoni okuti “chilichonse chili ndi nthawi; pali nthawi yolira komanso yosangalara”.

Related News
Malawi president under fire for family appointments to cabinet

New 31-member cabinet includes six figures who are related to each other, although not to the president. Malawians have voiced Read more

MARTHA CHIZUMA DECLARES WAR AGAINST CHAKWERA: SAYS PRESIDENT, JUDICIARY, ARMY AND POLICE CORRUPT

In a shocking tale to absorb, ACB boss Martha Chizuma has taken her corruption fight against her bosses, openly going Read more

Muluzi to represent Chakwera at former Zambia leader Rupiah Banda’s funeral

President Lazarus Chakwera has delegated former president and Malawi’s first president in the multiparty democracy Bakili Mluzi to represent him Read more

Honor Decision By President Lazarus Chakwera To Delegate Me

Former President Bakili Muluzi has described as an honor a decision by President Lazarus Chakwera to delegate him to represent Read more

Chakwera delegate Muluzi to represent Malawi at the burial of Rupiah Banda

Former President Bakili Muluzi has described as an honor a decision by President Lazarus Chakwera to delegate him to represent Read more

Chakwera committed to deal with challenges affecting private sector

President Lazarus Chakwera has committed to deal with challenges affecting the country's private sector investments such as land, legal and Read more

Govt Is Slow On Israel Embassy

Despite stating its intention to open a diplomatic mission in Israel, government has not appointed diplomats for the mission. The Read more

Former President Dr Bakili Muluzi Safely In Zambia To Attend Burial Of Rupia Banda

Former President Dr Bakili Muluzi with Zambian President Hakainde Hichilema as they pay their last respect to the late Rupiah Read more

Chakwera highlighted the importance of the Doha Programme

?? ???? ?? ????? ??? ???? ????????? ?? ??????- ????????? ????????

US Secretary of State commends Malawi for calling for withdrawal of Russian forces from Ukraine

```President Lazarus Chakwera yesterday held talks with United States Secretary of State, Antony Blinken, who commended Malawi’s clear calls for Read more

News To Read

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *