Thu. Apr 25th, 2024

Otsatira Chipani Cha UDF Wayamikira Chakwera Chifukwa Chothetsa Milandu Ya Muluzi

M’modzi mwa anthu otsatira chipani cha United Democratic Front ( UDF) , bambo John Black Dzuwa athokoza Pulezidenti wachipani cha Malawi Congress Party ( MCP) His Excellency Dr Lazarus McCarthy Chakwera yemwenso ndi Pulezidenti wadziko lino kaamba kolola kuti milandu ya Pulezidenti wakale wadziko lino Dr Bakili Muluzi ithe. Makhothi adziko lino athetsa milando yonse ya Dr Bakili Bakili Muluzi. Bambo John Black Dzuwa ati , Dr Bakili Muluzi adamangidwa kaamba kandale. A John Black Dzuwa atinso akuthokoza kuti dziko lapansi kuli anthu omwe amamva zinthu ndikupanga kuti Zikhale bwino. A John Black Dzuwa ati sadakhulupilire komanso kuyembekezera kuti chipani chomwe chingadzamasule Dr Bakili Muluzi mkukhala MCP. A John Black Dzuwa akuthokoza Pulezidenti wa MCP ( Dr Lazarus McCarthy Chakwera) komanso akuthokoza akuluakulu akumakhothi kaamba kothetsa milandu ya Atcheya His Excellency Dr Bakili Muluzi. Adzuwa akuti Zikomo !

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open