Thu. Apr 25th, 2024

Zaululika Kuti Mayi Colleen Zamba Amakakamiza Kampani Ya Nocma Kuti izichita Chinyengo

By Suleman Chitera Nov23,2022

“Mlembi wamkulu mu ofesi ya mtsogoleri wa dziko lino Colleen Zamba, amakakamiza bungwe la NOCMA kuti lichite chinyengo pogula mafuta.”

Izi zaululika lero pomwe yemwe anali ogwirizira udindo wa mkulu wa bungwe la NOCMA, Hellen Buluma, anakaonekera ku komiti ya nyumba yamalamulo yowona zakalembedwe ka ntchito ka anthu m’boma.

Buluma anati amakakamizidwa ndi Zamba kuti apereke mwai obweretsa mafuta mdziko muno kwa munthu wina wa dziko la Nigeria yemwe amangodziwika kuti Chief komanso munthu wina yemwe akuti ndi Evarista Kamwangala, yemwe akukhala ku South Africa.

Ngati wapampando wa bungwe la NOCMA, Zamba amayenera kuonekera ku komitiyi masanawa pamodzi ndi amnzake koma sanafike ndipo sanapereke chifukwa chilichonse.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open