CHIWELENGELO CHA ATSIKANA OTENGA MIMBA CHAKWERA KWAMBILI M’BOMA LA RUMPHI
Chiwelengelo chatsikana otenga mimba M’boma la Rumphi Chakwela Kufika pa 2234.
M’neneli wa Chipatala Cha Rumphi a
Banalori Mwamulima ati chiwelengelo ndichoyambila Mmwezi wa January kufika May M’chaka chino.
Read also: Mutharika hosts Enock Chihana at Beachside residence in Mangochi
Read also: Supporter Of Palestine War Chakwera loses Elections
Read also: FDH Bank plc, Ekhaya renew pact with Sunday Soirée
A Mwamulima ati nambayi ikusonyeza kuti chiwelengelo Chakwela ndi 4% maka pakati pa achitsana omwe ndi achichepele.
Wankulu wampando wa achinyamata a Misheck Msokwa ati Chiwelengelo Chawapatsa mantha.
Chiwelengelochi Chakwela kwambili kusiyana ndichaka chatha Chomwe Chinali 1618 Mmiyezi isanu.
Read also: Kalindo says he is following up an Indian case in Limbe
Read also: Twenty Ethiopians Arrested For Illegally Entering In The Country





