Mon. Apr 29th, 2024

Chilima Ndiye Ayimire Tonse Alliance 2025–Kaliati

Mlembi wamkulu wa chipani cha UTM Patricia Kaliati sabata latha anauza Malawi and world news kuti chomwe iwo akudziwa ndi choti President wawo Saulos Klaus Chilima ndi yemwe adzatsogolere Tonse Alliance pa chisankho cha President chaka cha mawa.

Mu mgwirizanowu muli zipani za UTM, MCP, PP ndi zina.

Kaliati wayankhula izi pomwe chipani cha MCP chinabwera poyera kuti President Lazarus Chakwera ndiyemwe adzaimire chipanichi pa chisankhocho.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

AGHF Feeds Patients, Guardians At Mangochi District Hospital

A giving hand foundation is a local organisation working in various programs in Malawi. On Thursday the organization together with Read more

NBM Donates K100 Million Towards Forest Restoration

National Bank of Malawi has committed K100 million for preservation and restoration of 6 natural resources in the country by Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open