Ndimulankhule Chakwera–Mutharika

Mtsogoleri wa chipani cha DPP Peter Mutharika wati ali ndi mau omwe akufuna kumuuza mtsogoleri wa dziko lino yemweso ndi mtsogoleri wa chipani cha MCP Lazarus Chakwera lachitatu likudzali.

Mutharika wayankhula izi kudzera kwa mneneri wake Shadrick Namalomba.

Poyankhula ndi MIJ Online Namalomba wati Mutharika ali ndi mau omwe akufuna kuuza Chakwera pa za kuvulazidwa kwa anthu otsatira DPP mu mzinda wa Lilongwe.

“Ngakhale a Mutharika akhale akuyankhula ku mtundu wa a Malawi Lachitatu lino pa ziwawa-zi koma kweni kweni uthenga-wu udzakhala ukupita kwa a Chakwera, ” watero Namalomba.

Namalomba wauza MIJ Online kuti ali ndi umboni ochuluka kuti chipani cha MCP ndi chomwe chavulaza otsatira DPP kaamba ka number plate ya galimoto yomwe inanyamula anthu-wo akuti mwini wake ndi wa MCP.

Padakali pano chipani cha MCP chakana kuti sichikukhudzidwa pa zipolowezi.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

David Bisnowaty former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country

Political cum and former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country https://youtu.be/S20UYlVcHs8

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window