1 min read

Chipani Cha DPP Agwirizana Kuti Nankhumwa akhalebe pampandowu.

Kusamvana komwe kunalipo m’chipani cha DPP pa yemwe akuyenera kukhala mkulu wa zipani zotsuta boma m’nyumba ya malamulo kwatha tsopano. Izi zikutsatira m’gwirizano omwe mbali zokhuzidwa zapanga kuti a Kondwani Nankhumwa akhalebe pampandowu. Malingana ndi mneneri wa chipani cha DPP, Shadrec Namalomba, a Nankhumwa akhalabe pa udindowu kufikira pomwe chipanichi chidzachititsenso chisankho china cha mtsogoleri […]

1 min read

Mutharika Threatens Legal Action Against Former Veep Khumbo Kachali

Former President Peter Mutharika and his Democratic Progressive Party are threatening to seek legal redress from courts against Former Vice President Khumbo Kachale over his alleged defamatory, malicious and damaging utterances Kachali reportedly alleged the DPP administration borrowed $350 million from the Afreximbank which it diverted into DPP officials through FDH Bank. Mutharika through his […]

1 min read

Seed-Co Partners Chakwera In Charity Golf Tourney

Picture: Seed-Co’s Sakurai Mbanda making a symbolic cheque presentation to Cathie Matura of the Presidential Charity Golf Tournament Organizing Committee Companies and individuals continue making donations towards the Presidential Charity Golf Tournament with Seed-Co Malawi being the latest with its K2.5 million financial support towards the initiative whose proceeds will go towards assisting needy tertiary […]

1 min read

Kodi Cholakwika Ndi Chani Ndi Ulendo Wa A Chakwera Okayankhula Ku America ?

Kunena moona khalidwe lotutana mudzi onse kunka nawo ku America sikuti tiwanamize a Malawi wayamba ndi boma la a Chakwera ai; koma ili ndi khalidwe lonyasa lomwe lakhala likusakaza ndalama za dziko lino ndima President onse omwe akhala akulamulira dziko lino oChakwera asanayambe kulamula dziko lino. Funso n’kumati kodi chavuta ndichani ndi ulendo wa oChakwera?Vuto […]