Tili Ku Bagamoyo komwe chilichonse chakwera ndi Chakwera – Mutharika

Mtsogoleri wakale wa dziko lino yemweweso ndi mtsogoleri wachipani chotsutsa boma cha Democratic Progressive -DPP Prof. Peter Munthalika wadzudzura boma la Dr. Lazarus Chakwera ati kamba kolephera kuyendetsa bwino dziko lino.

A Munthalika amalankhura izi masanawa pa msonkhano wa atolankhani omwe umachitikira kunyumba kwawo ku Mangochi.

Iwo ati ndizomvetsa chisoni kuti aMalawi akulephera kupeza zinthu zofunikira monga ziphaso zoyendera (passports)komaso ziphaso zoyendetsera galimoto.

Iwo ati ngakhale mavutowa alipo m’dziko muno aMalawi asadandaule ndipo asadere nkhawa chifukwa chipani chawo chakonzeka kudzamuliraso dziko lino akasankhidwa pa chisankho cha chaka chamawa.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Mustag Chothia, Sulema Ismael Karim In Land scam

Land remains one area that Malawians know has been heavily abused, characterised by ownership wrangles, not to mention corruption, fueled Read more

David Bisnowaty former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country

Political cum and former Member Of Parliament for Lilongwe City Centre break silence on political situation in the country https://youtu.be/S20UYlVcHs8

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window