Chilima Ndiye Ayimire Tonse Alliance 2025–Kaliati

Mlembi wamkulu wa chipani cha UTM Patricia Kaliati sabata latha anauza Malawi and world news kuti chomwe iwo akudziwa ndi choti President wawo Saulos Klaus Chilima ndi yemwe adzatsogolere Tonse Alliance pa chisankho cha President chaka cha mawa.

Mu mgwirizanowu muli zipani za UTM, MCP, PP ndi zina.

Kaliati wayankhula izi pomwe chipani cha MCP chinabwera poyera kuti President Lazarus Chakwera ndiyemwe adzaimire chipanichi pa chisankhocho.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

David Bisnowaty Israeli-Born Malawi Parliament Member: Actions, Not Words, Will Change Africa for the Better

Malawi MP David Bisnowaty. How does the Israeli-born son of an eastern European Holocaust survivor end up as a parliament Read more

Biography Of Zuneth Sattar

Zuneth Sattar Director of Xaviar Limited and Xaviar Investments Limited Zuneth Sattar is an experienced and knowledgeable property investor. With Read more

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

FDH Launch Islamic Banking Window