Malawi Freedom Network
Giving you daily news that rock the world
ExclusiveSports

‘A Malawi Musadandaule Taika chidwi pa world cup’_ watero Mabedi

Mphuzitsi wa timu ya mpira wamiyendo yadziko lino Patrick Mabedi wati tsopano agwilitsa ntchito masewela omwe atsala odzigulira malo mumpikisano wa Afcon ngati mbali yokozekela masewera odzigulira malo mumpikisano wapadziko lonse a World Cup.

A Mabedi ayankhula izi kutsatira pomwe timuyi yalephera kudzigulira malo mu mipikisano wa AFCON kutsatila kugonja ndi team ya Senegal 1-0 pamasewero omwe anachitika lero pabwalo la zamasewero la Bingu mu mzinda wa Lilongwe.

Malingana ndi a Mabedi ati timu yadziko linoyi siikuchita bwino kaamba kosakozekera bwino kotero masewero omwe atsalawa apeleka danga lokoza pomwe pakumavunda khola cholinga choti timuyi iyambe kuchita bwino.

Pakadali pano Flames ili pansi penipeni pa gulu L ndipo ilibe ngakhale point ndiimodzi yomwe kuchoka mumasewero anayi omwe yasewera.

Related posts

PDP To Go Solo In Next Year’s Polls

Malawi Freedom Network

Mivi iwiri yavulaza Mapale

Malawi Freedom Network

Gwengwe tours Pharmavova Malawi Limited in Blantyre

Malawi Freedom Network

Violence escalates in Khote Village as homes burn amid retaliatory attacks

Malawi Freedom Network

DPP Youth Leader Norman Chisale Criticizes MCP’s Richard Chimwendo Banda Over Response to Police Assault Case

By Suleman Chitera

Marc Bernal injury news

Malawi Freedom Network

Leave a Comment

Leave a review

This website uses cookies to improve your experience. We'll assume you're ok with this, but you can opt-out if you wish. Accept Read More