Mon. Apr 29th, 2024

Mpinganjira Walengeza Kuti Athandiza Achinyamata Ndi K18 Million

Wochita malonda Triephornia Mpinganjira walengeza kuti athandiza ndi K18 million achinyamata omwe akufuna kuchita malonda koma alibe kuthekera.

A Mpinganjira alengeza izi pa tsamba lawo la Facebook, ndipo ati iyi ikhala ndalama yothandiza achinyamatawo kuti apeze poyambira.

Kudzera mu ndondomekoyi, wachinyamata aliyense alandira K1 million atapereka pulani yabwino ya malonda omwe akufuna kuchita..

Malinga ndi a Mpinganjira, ndalama yokwana K1 million idzipelekedwa kwa m’nyamata m’modzi pa sabata ziwiri ndipo izi zikhala zikuchitika mpaka mwezi wa December chaka chino.

Achinyamata a zaka za pakati pa 18 ndi 35 ndi omwe akuyenera kutenga nawo gawo pa ndondomeko yomwe akuitcha: “Kuthandiza omwe alibe kuthekela kupita patsogolo”.

Related Posts

AGHF Feeds Patients, Guardians At Mangochi District Hospital

A giving hand foundation is a local organisation working in various programs in Malawi. On Thursday the organization together with Read more

NBM Donates K100 Million Towards Forest Restoration

National Bank of Malawi has committed K100 million for preservation and restoration of 6 natural resources in the country by Read more

Paramount Holdings Donates Medical Equipments To Area 25 Health Centre

Paramount Holdings Limited has handed over medical equipment worth 3 million Kwacha to Area 25 health centre. The organisation's Operations Read more

I am not a crook— Mulli

MAINTAINED THAT PROCEDURES WERE FOLLOWED—Mulli— Picture by Catherine Maulidi Businessperson and National Bus Services Chairperson Leston Mulli on Tuesday told Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open