Thu. Apr 25th, 2024

Atsikana Ambiri Atenga Mimba M’boma La Rumphi

By Suleman Chitera Jul11,2022

CHIWELENGELO CHA ATSIKANA OTENGA MIMBA CHAKWERA KWAMBILI M’BOMA LA RUMPHI

Chiwelengelo chatsikana otenga mimba M’boma la Rumphi Chakwela Kufika pa 2234.

M’neneli wa Chipatala Cha Rumphi a
Banalori Mwamulima ati chiwelengelo ndichoyambila Mmwezi wa January kufika May M’chaka chino.

A Mwamulima ati nambayi ikusonyeza kuti chiwelengelo Chakwela ndi 4% maka pakati pa achitsana omwe ndi achichepele.

Wankulu wampando wa achinyamata a Misheck Msokwa ati Chiwelengelo Chawapatsa mantha.

Chiwelengelochi Chakwela kwambili kusiyana ndichaka chatha Chomwe Chinali 1618 Mmiyezi isanu.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open