Wed. Apr 24th, 2024

Chakaka Nyirenda ali kokasaka komwe ndalama za AIP zidapita Zokwana k30 Billion Zomwe Lowe Anabetsa

By Suleman Chitera Nov11,2022

Mkulu wa malamulo m’dziko muno Thabo Chakaka Nyirenda ali m’dziko la Germany kusaka ndalama za amerika zokwana 543,000 zomwe zidasowa pomwe boma limafuna kugula feteleza

Chakaka Nyirenda wati ali kumeneko kulondoloza mapepala omwe athandizire pa kupezeka kwa ndalamazi

Boma la Malawi linabetsa ndalama zokwana K 750 million ku kampani ya Barkaat Foods Limited yomwe inkati igulitsa unduna wa zaulimi feteleza otsika mtengo

Lowe anatenga ndalama zokwana k30 Billion kupereka ku barkaat foods kuti agule fertilizer ndipo company ya barkaat foods inasowa ndi ndalamazo

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open