Mon. Apr 29th, 2024

Ma Banki apeza phindu lochuluka

Ma Banki asanu ndi atatu a m’dziko muno apanga phindu lokwana K256.7 billion m’chaka cha 2023 chokha, boma litadulapo kale msonkho.

Izi ndi malingana ndi lipoti la m’mene chuma chikuyendera m’dziko muno lochokera ku banki yayikulu pa dziko lonse (World Bank).

Lipotili lati phinduli lakwera kuchoka pa K170.8 billion lowe ma banki-wa anapeza m’chaka cha 2022.

Bankiyi yati ngakhale chuma cha dziko lino chakumana ndi mavuto ambiri, gawo la mabanki likupitilira kukwera komanso kupeza  phindu lochuluka.

Related Posts

The British NCA Operations In Malawi Remain Questionable, Britons Aim To Topple Tonse Government

Exposed! British NCA bankrolls PIJ to victimize successful business persons, politicians, judges in Malawi The truth be told! The establishment Read more

Mirece supports land reclamation bought by foreigners

Reverend Flywell Somanje…. this is the way to go A governance and human rights organization, the Millennium Information and Resource Read more

I am not a crook— Mulli

MAINTAINED THAT PROCEDURES WERE FOLLOWED—Mulli— Picture by Catherine Maulidi Businessperson and National Bus Services Chairperson Leston Mulli on Tuesday told Read more

Navicha appointed as a leader of opposition in parliament

Member of parliament for Thyolo Thava, Mary Thom Navicha has been recently appointed as a new leader of opposition following Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open