Ali Blessings Eid Agawa Ufa Ku Mabanja Omwe Akuvutika Ndi Njala
Olemba, Yusuf Daisa Anthu a mdera la Mangochi Masongola kwa Senior Chief Jalasi, ayamikira Ali Blessings Idi yemwe akupikisana paudindo wa phungu wakunyumba yamalamulo, chifukwa chogawa ufa ku mabanja 500…
