Mon. Apr 29th, 2024

Zavotereni DPP kuti Mupulumutse Dziko Ku Mbava

Mtsogoleri wa chipani cha DPP a Peter Mutharika wapempha anthu a m’boma la Balaka kuzavotela chipanichi ngati akufuna chitukuko.

A Mutharika ati iwo adzapitiliza zitukuko zonse zimene anaziyamba.

Iwo ati adzapitilizanso kupereka chakudya kwa anthu omwe pakadalipano akhudzidwa ndi njala.

A Mutharika amema anthu a m’delali kuti akhale ndi chiphaso chaunzika komanso adzalembetse mu kaundula wa oponyera voti kuti adzathe kutenga nawo gawo pa chisankhochi.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

Navicha appointed as a leader of opposition in parliament

Member of parliament for Thyolo Thava, Mary Thom Navicha has been recently appointed as a new leader of opposition following Read more

Govt Refutes Speculations Spreading On Social Media On Sattar Contracts

Minister of Information and Digitisation Moses Kunkuyu has justified the government’s decision to initiate a $19 million (about K32.3 billion) Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open