Mon. Apr 29th, 2024

2025 Dr Saulos Chilima Azapezeka Pa Ballot Paper Ngati Mtsogoleri wa Tonse Alliance

NJAWALA WATI MGWILIZANO WA CHAKWERA NDI CHILIMA UNACHITIKA PAMASO PAKHOTI

Pamene Chipani cha Malawi Congress Party MCP chasakha Dr Lazarus chakwera Ngati yemwe atazawaimilire pachisakho cha 2025. Koma Mlembi ku Chipani cha UTM a Felix Njawala ati
Kusakhidwa kwa a Chakwera ndizakubanja lawo la MCP.

Malingana ndi a Njawala ati “Mungwirizano wa Tonse Alliance pali Dr saulos Chilima
Malingana ndizomwe anthu awiriwa anagwirizana ife sitikututumuka”.

A Njawala anapitilira kunena kuti “Ngwirizano wawo unachitika pamaso pa Khoti
Ndipo ndisindike pano Kuti 2025 Dr Saulos Chilima azapezeka pa Ballot Paper Ngati Mtsogoleri wa Tonse Alliance”.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi business tycoon Simbi Phiri disassociates himself from forming up “Congress for Democrats”

Business Mogul Simbi Ashan Phiri who is Executive Chairman of Katho Civils has disassociated himself from social media rumours that Read more

Navicha appointed as a leader of opposition in parliament

Member of parliament for Thyolo Thava, Mary Thom Navicha has been recently appointed as a new leader of opposition following Read more

Jumah says it is possible to change Malawi in 10-15 years

By Vincent Gunde President and Commander in Chief of Muvi wa Chilungamo Revolutionary Party (MRP) Bantu Saunders Jumah, says it Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open