Tue. Apr 30th, 2024

MCP Yati Dpp Inkapwanya Dala Malamulo

By Suleman Chitera Nov25,2022

Chipani cha MCP chati chikudziwa bwino kuti kuwonjezera madera a phungu komanso makhansala kufuna ndalama zochuluka komabe nkofunika mogwirizana ndi malamulo kuti ganizo la bungwe la MEC ligwire ntchito basi.

M’neneri wa chipanichi, Maurice Munthali wadzudzulanso chipani cha DPP ati posafuna kulemekeza malamulo m’mbuyomu ponena kuti zimapangitsa kuti anthu asamalandire zitukuko mofanana.

Posachedwapa, nyumba ya malamulo idavomereza lipoti la MEC lowonjezera madera a aphungu kuchoka pa 193 kufika pa 229 ndipo madera a makhansala afika pa 509 kuchoka pa 462.

Koma DPP yati kuwonjezera maderawa nkusaganiza kamba koti pakadalipano dziko lino likudutsa kale m’mavuto adzaoneni pachuma.

Related Posts

DPP Blues Rebels Brings Division In

DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open