Friday, December 1Malawi's top news source
Shadow

MCP Yati Dpp Inkapwanya Dala Malamulo

Chipani cha MCP chati chikudziwa bwino kuti kuwonjezera madera a phungu komanso makhansala kufuna ndalama zochuluka komabe nkofunika mogwirizana ndi malamulo kuti ganizo la bungwe la MEC ligwire ntchito basi.

M’neneri wa chipanichi, Maurice Munthali wadzudzulanso chipani cha DPP ati posafuna kulemekeza malamulo m’mbuyomu ponena kuti zimapangitsa kuti anthu asamalandire zitukuko mofanana.

Posachedwapa, nyumba ya malamulo idavomereza lipoti la MEC lowonjezera madera a aphungu kuchoka pa 193 kufika pa 229 ndipo madera a makhansala afika pa 509 kuchoka pa 462.

Koma DPP yati kuwonjezera maderawa nkusaganiza kamba koti pakadalipano dziko lino likudutsa kale m’mavuto adzaoneni pachuma.

Giving you more news Malawi Freedom Network News

Mkaka ali pamoto powaletsa otsatira MCP kuti asakumane ndi Chakwera

Mlembi wamkulu wa chipani cha Malawi Congress (MCP) Eisenhower Mkaka yemwenso ndi nduna yowona za chilengedwe wadzudzulidwa kamba koletsa anthu Read more

APM Says DPP To Return In Power In 2025

The former president of Malawi, Peter Mutharika, who is also the leader of Democratic Progressive Party (DPP) has assured Malawians Read more

Mutharika Breaks Silence On Infighting In DPP

Former President Peter Mutharika who is also leader of the opposition Democratic Progressive Party (DPP) has assured party supporters that Read more

MCP Youth Member Blast MCP And Ready To Spill The Bean

Malawi Congress Party (MCP) Member Chipiliro Kaliyopa, who is also a suspect in the Police 'recruits' case has refuted claims Read more

Police Hunting Chipiliro Kaliyopa

Police in Lilongwe are hunting for Chipiliro Kaliyopa, a man suspected to have duped Malawi Congress Party MCP youth league Read more

DPP Secretary General Grezelder Jeffrey Hits Critics

Democratic Progressive Party (DPP) secretary general (SG) Grezelder Jeffrey has refuted reports that the rally scheduled for Sunday at Mgona Read more

Norman Chisale To Contest As DPP National Youth Director

Former Malawi President Peter Mutharika top aide Mr Norman Paulos Chisale joins frontline politics. Information gathered indicates that Chisale wants Read more

Dpp To Restore The Lost Economy 2025-Magonjwa

Democratic Progressive Party (DPP) Member of Parliament for Machinga South East Fyness Mangonjwa has said the party is geared to Read more

ACB caught pants down judge-shopping in Zomba

Malawi courts have stated time without number for parties to litigation to avoid judge shopping yet the vice seems to Read more

DPP NORTH FOR MUTHARIKA – VUWA

Nkhata-Bay Central Parliamentarian and Chief Whip in Parliament Symon Vuwa Kaunda has endorsed their party President Prof. Arther Peter Mutharika Read more

News To Read

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *