Sat. Apr 20th, 2024

Mafuta A Galimoto Avuta

By Suleman Chitera Jun22,2022

Vuto lakusowa kwa mafuta a galimoto likupitilira kukhudza maboma ambiri ndipo boma la Ntcheu, oyendetsa galimoto kumeneku akukhala m’mizere kuti agule mafutawa.

Izi zakakamiza oyendetsa njinga zamoto kukweza mtengo onyamulira anthu akakwera njingazi kuzungulira pa boma ndi ndalama yokwana K500 yoonjezera, malinga ndi a Davie Maganga.

MFN Online itayendera malo anayi omwe amagulitsako mafuta a galimoto pa boma ku Ntcheu, malo a Petroda okha ndiomwe anali ndi mafuta a mtundu wa Diesel okha.

Masiku apitawa, wachiwiri kwa mkulu wa bungwe la National Oil Company of Malawi-NOCMA a Hellen Buluma anauza Zodiak Online kuti dziko lino lili ndimafuta okwanira ndipo vutoli ladza kaamba kampani zogulitsa mafuta zina zikulephera kunyamula mafutawa.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

President Lazarus Chakwera has officially opened the Blantyre International Cancer Centre, The private health facility, has been constructed by the Thomson and Barbara Mpinganjira Foundation