Charles Kamanga wachita mutu wa zizwa ndi osewera ake.
Mphunzitsi wamkulu wa timu ya Kamuzu Barracks, Charles Kamanga, wadandaula kuti osewera ake ena akusewera ngati sakufuna. Izi wayankhula kutsatira Kukhadzulidwa 2-0 ndi a nkhondo anzawo kuchokera ku Kaning’ina, Moyale…
