Mtsogoleri wa chipani cha MCP Dr. Lazarus Chakwera wadzudzula omwe akumalowetsa imfa ya wachiwiri kwa mtsogoleri wadziko lino wakale Dr. Saulos Chilima munkhani za ndale.
Iwo ati anthu atenge zomwe zidatuluka mulipoti la akatswiri am’dziko la Germany komanso madotolo a m’dziko muno zokhudza ngozi ya ndege yomwe idapha a Chilima ndi anthu ena 8.
Mtsogoleriyu wati iwo ndi a Chilima anagwilizana zopanga ndale zotukula miyoyo ya a Malawi osati ndale zopakana matope.
Iwo ati ndi mtsogoleri yemwe wachita zitukuko zosiyanasiyana m’dziko muno ndipo athokoza anthu achipanichi powapasanso mwayi oti apitilize kutsogolera chipanichi.
Related posts:
Nine Women Rise: 2025 Elections Mark Historic Shift Toward Gender-Inclusive Leadership
Latest
100 Days of Promise: Youths Hail Mutharika’s Early Gains, Urge Fiscal Discipline
Latest
Gabadinho Mhango Eager to Start Fresh Chapter with Flames
Latest
FINCA Malawi Reports 226% Profit Surge in 2025, Expands Loans and Rural Financing
Business
Mzuzu University promotes wellness of staff members through sports
Latest
A new dawn for Malawi: Why Kabambe and Mtumbuka are the right choice
Latest


