Anzake kunjaku ndi a church omwenso amadalira kupempha.
President wakale wa dziko lino Mai Joyce Banda ati Dr Lazarus McCarthy Chakwera alibe network ya maiko akunja nkana mafuta ndi forex zikusowa mdziko muno.
Iwo amayankhula izi pa pulogalamu ya Kwagwanji pa Times Tv ndi anyamata atatu,Brian Banda, Wonder Msiska komanso Jonna Mpakuku.
Mai Banda adapitiliza kunena kuti mdziko lino liri pa moto wadzaoneni chifukwa a Chakwera alibe maubale ndi ma President akunja (Network alibe) choncho mafuta avutabe.
Read also: MUBAS To Construct 10,000 Hostels
Read also: Government’s bold move ahead of September 16 Elections: Promotion of all primary school teachers
Read also: Onjezani Kenani urges Malawians to register and vote responsibly

