Tue. Apr 23rd, 2024

NDIZABWEZELESA UMODZI CHIPANI CHA DPP ATERO A BRIGHT MSAKA

By Suleman Chitera Aug15,2022

a Msaka ati ngati iwo adzasankhidwe kukhala mtsogoleli wa chipani cha DPP mchaka cha 2023, maso awo adzakhala kudzapambana pa chisankho cha utsogoleli wa dziko cha mchaka cha 2025.

Iwo ati ali ndi khumbo lobwezeretsa umodzi mchipani cha DPP akawina pa mpandowu.

Iwo atinso cholinga chawo ndikudza konzanso chuma cha dziko lino chomwe ati chasokonekera pakanali pano.

“Ichi ndichiyambi cha Malawi wokonzeka” Msaka.

Related Posts
DPP Blues Rebels Brings Division In
DPP Blues Rebels Brings Division In

The way Charles Mchacha is castigating the Leader of Opposition in Parliament, Hon Kondwani Nankhumwa, is just testimony enough that Read more

Malawi Freedom Network advice President Banda to fight corruption

If you thought Malawians are lazy people, I bet you a Dinosaur, think twice and you will know, check in Read more

Malawi Government Faulted Over Arrests of Coup Suspects

The recent arrest in Malawi of three opposition politicians accused of planning to unseat President Peter Mutharika is dissent from Read more

Allegations of a coup plot sour diplomatic ties

The US embassy has denied involvement in an alleged plot to overthrow the president, Peter Mutharika. Analysis Media reports that Read more

Other stories

Leave a Reply

Your email address will not be published. Required fields are marked *

Ekhaya luxury Resort fully open