a Msaka ati ngati iwo adzasankhidwe kukhala mtsogoleli wa chipani cha DPP mchaka cha 2023, maso awo adzakhala kudzapambana pa chisankho cha utsogoleli wa dziko cha mchaka cha 2025.
Iwo ati ali ndi khumbo lobwezeretsa umodzi mchipani cha DPP akawina pa mpandowu.
Iwo atinso cholinga chawo ndikudza konzanso chuma cha dziko lino chomwe ati chasokonekera pakanali pano.
“Ichi ndichiyambi cha Malawi wokonzeka” Msaka.
Read also: PAC Slams Police Silence on Lilongwe Protest Arrests, Demands President’s Action
Read also: President Chakwera returns from official UAE visit focused on fuel procurement and bilateral talks
Read also: Lions Club of Mandala Partners with National Bank of Malawi to provide free health screenings

