Kutsatira mvula yochuluka imene inadza kamba ka Namondwe wa Freddy, nyanja ya Chilwa ku Zomba yadzadza pomwe madzi tsopano afika midzi yoyandikana ndi nyanjayi.
Malingana ndi a Fanuel Sadik, amene amakhala kuderali, madzi afika midzi yoyandikila doko la Kachulu komanso Mchenga ndipo anthu asamukira madera ena.
Khansala waderali, a Douglas January, anatsimikiza izi ndipo anati pakali pano kufika kunyanjaku pagalimoto ndikosatheka.
Zithuzi zikuonetsa momwe zinthu ziliri ku nyanjayi.
Read also: 3 People Missing After Crocodile Attacks In Nsanje
Read also: 70 Year Old Woman Wins Grand prize in the FDH ‘Kukonza Tsogolo’ promotion
Read also: Alfred Jiya Withdraws Complaint from MEC as Election Disputes Deepen in Nankhaka Constituency

