CHIWELENGELO CHA ATSIKANA OTENGA MIMBA CHAKWERA KWAMBILI M’BOMA LA RUMPHI
Chiwelengelo chatsikana otenga mimba M’boma la Rumphi Chakwela Kufika pa 2234.
M’neneli wa Chipatala Cha Rumphi a
Banalori Mwamulima ati chiwelengelo ndichoyambila Mmwezi wa January kufika May M’chaka chino.
A Mwamulima ati nambayi ikusonyeza kuti chiwelengelo Chakwela ndi 4% maka pakati pa achitsana omwe ndi achichepele.
Wankulu wampando wa achinyamata a Misheck Msokwa ati Chiwelengelo Chawapatsa mantha.
Chiwelengelochi Chakwela kwambili kusiyana ndichaka chatha Chomwe Chinali 1618 Mmiyezi isanu.
Read also: BMTV claims MCP was a government of experiment not experience
Read also: GROUP VILLAGE HEAD SPENDS NIGHT IN COOLER FOR FORGERY
Read also: Pressure Mounts On ACB To Probe HTD Owner Abdul Aboobaker’s corrupt Dealings

