By Comrade jumbe
Pa chichewa pali mawu amatero kuti tsogolo ndi la iwo amene akukonzekera lero ,
Abale ndi alongo lero ndi mwayi wina wofunikira kwambiri kwa nzika iliyonse yomwe ikufunira zanwino dziko lino .
Mmene kalembera wa zisankho afika ku mapeto uwu ndi mwayi wathu womaliza wokonzekera kusintha komwe tonse amalawi takhala tikuyembekezera.
Chisankho chomwe chikubwerachi sichinthu chongochitika mwachizoloŵezi monga mwa nthawi zonse koma ndi nthawi yofunika kwambiri m’mbiri ya dziko lathu.
Kukhala chete osatenga nawo gawo liri lonse pa chisanko pamene ena akusankha tsogolo lathu ndi kuzimpwanyila tokha ufulu okonza tsogolo la dziko lathu chifukwa mphamvu zobweretsa kusintha zili mu voti yathu ndipo uwu ndi mwayi wotsiriza popeza kulembetsa kwa mec kwafika kumalecheleche.
Tiyenela kukumbukira kuti mtsinje umadzadza ndi dontho limozi limozi kulembetsa kwanu kungawoneke ngati kochepa koma kukalumikizana ndi mamiliyoni ena kumakhala mphamvu yomwe palibe munthu olo boma linganyalanyaze.
Ndikumema inu nonse amalawi kuti pitani mukalembetse mukawundula wazisankho auzeni anzanu akubanja lanu ndi aneba kuti achitenso chimodzimodzi.uwu ndi mwayi wathu kuti tichotse omwe alephera ndikusankha atsogoleri omwe adzayike miyoyo ya anthu patsogolo.
Chisankho cha mu September sichisankho chabe chifukwa amalawi talira kokwana ndipo tikulira kotero ndi nthawi yathu yobweretsa kusintha komwe takhala tikudikirira.
Kalembetseni lero ndikuteteza liwu lanu pokonza tsogolo la dziko lathu. mphamvu ili m’manja mwathu tiyeni tigwiritseni ntchito mwanzeru .
pamodzi tingathe
- NBM plc donates K10 million to IMM lake conference
- Kasungu chiefs decry ESCOM transformer vandalism
- Press Cane starts organic fertiliser production
- Rhodrick Junaid Kalumpha Steps Up to Restore Cooking at Mangochi District Hospital
- CCM-PPM Demands NOCMA Board Dissolution Over K700 Million Transfer
- Let Us Be Honest With One Another: Malawi Was Blessed With APM
- 22nd Agriculture Fair Opens in Blantyre as Malawi Pushes Agricultural Transformation
- Study Raises Concerns Over Political Representation of Muslims and Yaos in MCP and DPP Governments
- Kafukufuku Wadzudzula MCP ndi DPP pa Kugwiritsa Ntchito Asilamu ndi Ayao pa Ndale
- NOCMA K700 Million Fuel Payment Dispute Raises Questions as NAPP Demands Answers
- NOCMA Deputy CEO Micklas Reuben Arrested Over Alleged $403,615 Fuel Transaction
- Zambian Law Association condemns courts shutdown
- Lilongwe to Launch First City-Wide Electric Public Bus System
- Mozambique Police Stations Turned Into Scrapyards as Impounded Vehicles Rot for Decades
- UNIMA Students Left in Loan Limbo as August 29 Appeals Deadline Nears
- Football Legends Association Raises K192 Million as Simama Hotels, Austo Add K8 Million
- US Eyes Greater Investment in Malawi as American Chamber of Commerce Launches
- BREAKING: Former Electoral Body Chief Andrew Mpesi Arrested
Read also: Chakwera Fires DPP Steven Kayuni Over Unsound Judgment
Read also: Why Are Traffic Police Officers So Corrupt?












