Anzake kunjaku ndi a church omwenso amadalira kupempha.
President wakale wa dziko lino Mai Joyce Banda ati Dr Lazarus McCarthy Chakwera alibe network ya maiko akunja nkana mafuta ndi forex zikusowa mdziko muno.
Iwo amayankhula izi pa pulogalamu ya Kwagwanji pa Times Tv ndi anyamata atatu,Brian Banda, Wonder Msiska komanso Jonna Mpakuku.
Mai Banda adapitiliza kunena kuti mdziko lino liri pa moto wadzaoneni chifukwa a Chakwera alibe maubale ndi ma President akunja (Network alibe) choncho mafuta avutabe.
Read also: Opposition Political Parties to Hold Joint Press Briefing Ahead of 2025 General Elections
Read also: Activist Agape Khombe Calls for Broad-Based Inquiry into Chilima Plane Crash
Read also: Peter Mutharika: The Patriot President Malawi Still Misses

